Frend

Frend

Share

Reminding the ummah all praise is due to Allah who teaches a person things he doesn't know..

01/06/2026

Osamuka! Osamuka! aiwala ujeni padenga🤣🤣

06/05/2026

Akumati ndi ma graduate.
Alinawotu ma degree.
Amati ndi ophunzira iwowo.
Chipanda chodzadza ndi utoto wa maphunziro adamwera iwowo.
Amati ndi ozindikiratu iwowo.
Anawerengatu ma book ochuluka.
Amadziwa zinthu zosiyanasiyana.
Koma zoti chisilamu n'chipembedzo monga chilichonse.
Si chilankhuro komaso mtundu wa munthu.
Koma n'chipembedzo cha aliyense.
Sadziwatu iwowo.
Aliyense ooneka mwa chiluya.
Ooneka mwa chimwenye ndinso mwa chiyao.
Okhala nalo dzina lomveka mwa chiluya.
Olankhura chiluya ndinso chiyao.
Ameneyotu ndi msilamu kwa iwowo.
Zoti Arabic ndinso chiyao.
Ndichilankhuro monga chingerezi, chipwitikizi ndinso chichewa.
Sadziwatu iwowo.
Komatu iwowo, amati ndi ophunzira.
Amati ndi ozindikiratu iwowo..... .............to be continued


Rafiq Saidi Assami
MAV TALK SHOW
Indee Voices
Hûssêíñ Mâílôs
Brown Chrispine

23/03/2026

Ineyo nduona ngati mnyamatayu za ma nasheed zija zinkamuchedwetsa, inu muona bwa? 🤣

Omar Ussi zabho?

Want your public figure to be the top-listed Public Figure in Lilongwe?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Category

Address

Chilinde
Lilongwe