Islamic Guide Malawi
this is an islamic page the place where we advise fellow muslims islamically
Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh!!!!!!
Kuyamikidwa konse ndikwa Allahu Taala mafuno Abwino apite kwa mtumiki saw a kubanja kwake komanso ndi masahabah ake.
LERO TIYENI TIPHUNZIRE ZA TWAHARAH.
๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ๐๏ธ
Twaharah ndi liwu la Chiarabu lomwe tanthauzo lake ndi kuyera kapena kuti Ubwino wa kusakhala ndi umve ulionse.
Ndipo Twaharah imayang'anidwa mmagawo anayiโคต๏ธ
1 Twaharah yapathupi
2 Twaharah yamuzovala
3 Twaharah yammadzi
4 Twaharah ya pamalo oswalira
Choncho mitundu imafunika kuilabadila pa nthawi yomwe tikupanga za Twahara
Mtumiki saw Adalankhula kuti,
ุฃูุทููุฑ ุดุทุฑ ุงูุฅูู
ุงู
Ndithu ukhondi ndigawo lachikhulupiliro chachislamu.
๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด๐ด
Komanso Mtumiki saw adalankhulanso kuti, โคต๏ธ
ุฃูุทููุฑ ู
ูุชุงุญ ุงูุตูุงุฉ
Ukhondo(kuziyeretsa) ndimakiyi aswalah
Choncho msilamu kuti akhale wa chire watayali pa ibadah akuyenera kukhala waukhondo nthawi zonse.
Nde mmene tafotokozera poyamba muja
Twaharah tikuyenera kuyang'ana mmagawo anayi amenewa.
Ungathe kukhala nditwahara yapathupi koma zovala zilibe Twaharah zikatero swalah sizingatheke.
Utha Kukhala nditwahara m'thupi ndimuzovala koma Malo oswalira ndikukhala opanda Twaharah,
Kapena tingathe kukhala oti tasamba bwinobwino komanso tachapa bwinobwino koma ndikukhala opanda Twaharah chifukwa cha madzi omwe tagwilitsa ntchito anali opanda Twaharah.................................
Ikupitilira
Pangani like kapena comment post yi kuti tidziwe kuti tikamapanga post awerengi alipo ndipo ife tudzalimbikitsika pomalembapo zambiri pa page pano
#
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Telephone
Address
Area 49
Lilongwe